Kodi mumakonda Ambuye?Limeli ndi funso lofunika kwambiri! Ambuye athu, Yesu Khristu, anafunsa Petro kuti, "Petro, umandikonda?" N'chifukwa chiyani chikondi chanu pa Mulungu chiri chinthu chimene tiyenera kukambirana?Yesu akunena kuti lamulo lalikulu kwambiri ndi lakuti: "Uzikonda Ambuye Mulungu wako, ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi nzeru zako zonse." Nthawi zina, pamakhala zochitika zimene Ambuye amalola kuti zibwere pamoyo panu-zochitika zimene zimangokhala mayeso, mayeso otsimikizira chikondi chanu kwa Ambuye.
Ngati mumakonda Ambuye, tsimikizani chikondi chanu mwa kupambana mayeso a chikondi!Buku lina lodabwitsa lolembedwa ndi wolemba wodziwika bwino, Dag Heward-Mills, lidzakupangitsani kuganiza mozama ndi kudzifunsa funso lofunika koposa: "Kodi ndimamukonda Ambuye kwenikweni?"
Kodi mumakonda Ambuye?Limeli ndi funso lofunika kwambiri! Ambuye athu, Yesu Khristu, anafunsa Petro kuti, "Petro, umandikonda?" N'chifukwa chiyani chikondi chanu pa Mulungu chiri chinthu chimene tiyenera kukambirana?Yesu akunena kuti lamulo lalikulu kwambiri ndi lakuti: "Uzikonda Ambuye Mulungu wako, ndi mtima wako wonse, ndi moyo wako wonse, ndi nzeru zako zonse." Nthawi zina, pamakhala zochitika zimene Ambuye amalola kuti zibwere pamoyo panu-zochitika zimene zimangokhala mayeso, mayeso otsimikizira chikondi chanu kwa Ambuye.
Ngati mumakonda Ambuye, tsimikizani chikondi chanu mwa kupambana mayeso a chikondi!Buku lina lodabwitsa lolembedwa ndi wolemba wodziwika bwino, Dag Heward-Mills, lidzakupangitsani kuganiza mozama ndi kudzifunsa funso lofunika koposa: "Kodi ndimamukonda Ambuye kwenikweni?"